Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 5:25 - Buku Lopatulika

25 Mphulupulu zanu zachotsa zimenezi, ndi zochimwa zanu zakukanitsani inu zinthu zabwino.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Mphulupulu zanu zachotsa zimenezi, ndi zochimwa zanu zakukanitsani inu zinthu zabwino.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Koma zolakwa zanu zaletsetsa zonsezi, ndipo machimo anu akumanitsani zokoma.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Koma zolakwa zanu zalepheretsa zonsezi; ndipo machimo anu akumanitsani zabwino.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 5:25
11 Mawu Ofanana  

Anthu opusa azunzika chifukwa cha zolakwa zao, ndi chifukwa cha mphulupulu zao.


Dziko la zipatso, likhale lakhulo, chifukwa cha choipa cha iwo okhalamo.


koma zoipa zanu zakulekanitsani inu ndi Mulungu wanu; ndipo machimo anu abisa nkhope yake kwa inu, kuti Iye sakumva.


Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya onena za chilala.


Zingakhale zoipa zathu zititsutsa ife, chitani Inu chifukwa cha dzina lanu, Yehova; pakuti zobwerera zathu zachuluka; takuchimwirani Inu.


Ndipo mvula yakanidwa, ndipo panalibe mvula ya masika; ndipo unali ndi nkhope ya mkazi wadama, unakana manyazi.


Njira yako ndi ntchito zako zinakuchitira izi; ichi ndicho choipa chako ndithu; chili chowawa ndithu, chifikira kumtima wako.


Kodi munthu wamoyo adandauliranji pokhala m'zochimwa zake?


Mphulupulu yako yatha, mwana wamkazi wa Ziyoni, Yehova sadzakutenganso ndende; koma adzazonda mphulupulu yako, mwana wa mkazi wa Edomu, nadzavumbulutsa zochimwa zako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa