Yeremiya 5:25 - Buku Lopatulika25 Mphulupulu zanu zachotsa zimenezi, ndi zochimwa zanu zakukanitsani inu zinthu zabwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Mphulupulu zanu zachotsa zimenezi, ndi zochimwa zanu zakukanitsani inu zinthu zabwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Koma zolakwa zanu zaletsetsa zonsezi, ndipo machimo anu akumanitsani zokoma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Koma zolakwa zanu zalepheretsa zonsezi; ndipo machimo anu akumanitsani zabwino. Onani mutuwo |