Yeremiya 5:23 - Buku Lopatulika23 Koma anthu awa ali ndi mtima woukirana ndi wopikisana; anapanduka nachoka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Koma anthu awa ali ndi mtima woukirana ndi wopikisana; anapanduka nachoka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Koma anthu ameneŵa ndi okanika ndiponso a mtima waupandu. Adapatuka ndipo adapitiratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Koma anthu awa ndi nkhutukumve ndiponso a mitima yowukira; andifulatira ndipo andisiyiratu. Onani mutuwo |