Yeremiya 5:21 - Buku Lopatulika21 Tamvanitu ichi, inu anthu opusa, ndi opanda nzeru; ali ndi maso koma osaona, ali ndi makutu koma osamva; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Tamvanitu ichi, inu anthu opusa, ndi opanda nzeru; ali ndi maso koma osaona, ali ndi makutu koma osamva; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 “Imvani izi, inu anthu opusa, opanda ndi nzeru zomwe, inu amene maso muli nawo, koma simupenya, amene makutu muli nawo, koma simumva. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Imvani izi, inu anthu opusa ndi opanda nzeru, inu amene maso muli nawo koma simupenya, amene makutu muli nawo koma simumva. Onani mutuwo |