Yeremiya 5:20 - Buku Lopatulika20 Nenani ichi m'nyumba ya Yakobo, lalikirani mu Yuda, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Nenani ichi m'nyumba ya Yakobo, lalikirani m'Yuda, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Mulalike kwa ana a Yakobe, mulengeze kwa anthu a ku Yuda kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “Lengeza izi kwa ana a Yakobo ndipo mulalikire kwa anthu a ku Yuda kuti, Onani mutuwo |