Yeremiya 49:9 - Buku Lopatulika9 Akafika kwa inu akutchera mphesa, sadzasiya mphesa zokunkha? Akafika usiku akuba, adzaononga mpaka kutha? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Akafika kwa inu akutchera mphesa, sadzasiya mphesa zokunkha? Akafika usiku akuba, adzaononga mpaka kutha? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Othyola mphesa akadakwera kwa inu, akadakusiyiraniko mphesa pa nthambi. Mbala zikadafika usiku, bwenzi zitangotengako zofunikira zokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kodi anthu othyola mphesa akanafika kwa inu akanakusiyiraniko mphesa pangʼono pokha? Anthu akuba akanafika usiku akanangotengako zimene akuzifuna zokha? Onani mutuwo |