Yeremiya 49:8 - Buku Lopatulika8 Thawani inu, bwerani, khalani mwakuya, inu okhala mu Dedani; pakuti ndidzatengera pa iye tsoka la Esau, nthawi yoti ndidzamlanga iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Thawani inu, bwerani, khalani mwakuya, inu okhala m'Dedani; pakuti ndidzatengera pa iye tsoka la Esau, nthawi yoti ndidzamlanga iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Anthu a ku Dedani bwererani, thaŵani mukakhale ku makwaŵa. Ndithudi ndidzalanga zidzukulu za Esau pa tsiku lake la chiweruzo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Inu anthu a ku Dedani, thawani, bwererani ndi kukabisala ku makwalala chifukwa ndidzagwetsa mavuto pa zidzukulu za Esau popeza nthawi yawo ya chiweruzo yafika. Onani mutuwo |