Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 49:6 - Buku Lopatulika

6 Koma pambuyo pake ndidzabwezanso undende wa ana a Amoni, ati Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Koma pambuyo pake ndidzabwezanso undende wa ana a Amoni, ati Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Komabe pambuyo pake ndidzaŵabwezera ufulu Aamoni,” akutero Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 “Komabe pambuyo pake, ndidzabwezera kwawo Aamoni,” akutero Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 49:6
8 Mawu Ofanana  

Malonda ake ndi mphotho yake zidzakhala zopatulikira Yehova; sizidzasungidwa kapena kuikidwa; chifukwa malonda ake adzakhala kwa iwo, amene akhala pamaso pa Yehova, kuti adye mokwana, navale chaulemu.


Ndipo padzakhala kuti nditazula iwo, ndidzabwera, ndipo ndidzawachitira chisoni; ndipo ndidzabwezanso iwo, yense ku cholowa chake, ndi yense kudziko lake.


ndipo ndidzawapereka m'manja a iwo amene afuna moyo wao, ndi m'dzanja la Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni, ndi m'manja a atumiki ake; pambuyo pake adzakhalamo anthu, monga masiku akale, ati Yehova.


Koma ndidzabwezanso undende wa Mowabu masiku akumaliza, ati Yehova. Ziweruzo za Mowabu ndi zomwezi.


Koma padzaoneka masiku akutsiriza, kuti ndidzabwezanso undende wa Elamu, ati Yehova.


Ndipo ndidzabweza undende wao, undende wa Sodomu ndi ana ake, ndi undende wa Samariya ndi ana ake, ndi undende wa andende ako pakati pao;


Adzalowanso m'dziko lokometsetsalo ndi maiko ambiri adzapasuka; koma opulumuka dzanja lake ndi awa: Edomu, ndi Mowabu, ndi oyamba a ana a Amoni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa