Yeremiya 49:4 - Buku Lopatulika4 Chifukwa chanji udzitamandira ndi zigwa, chigwa chako choyendamo madzi, iwe mwana wamkazi wobwerera m'mbuyo, amene anakhulupirira chuma chake, nati, Adza kwa ine ndani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Chifukwa chanji udzitamandira ndi zigwa, chigwa chako choyendamo madzi, iwe mwana wamkazi wobwerera m'mbuyo, amene anakhulupirira chuma chake, nati, Adza kwa ine ndani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chifukwa chiyani mukunyadira zigwa zanu, inu anthu osakhulupirika, amene munkadalira chuma chanu nkumati, ‘Ndani angalimbane ndi ife?’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Chifukwa chiyani mukunyadira chigwa chanu, inu anthu osakhulupirika amene munadalira chuma chanu nʼkumati: ‘Ndani angandithire nkhondo?’ Onani mutuwo |