Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 49:30 - Buku Lopatulika

30 Thawani inu, yendani kutali, khalani mwakuya, Inu okhala mu Hazori, ati Yehova; pakuti Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni anapangira uphungu pa inu, nakulingalirirani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Thawani inu, yendani kutali, khalani mwakuya, Inu okhala m'Hazori, ati Yehova; pakuti Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni anapangira uphungu pa inu, nakulingalirirani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Inu anthu a ku Hazori, thaŵani, fulumirani, kabisaleni ku makwaŵa. Nebukadinezara, mfumu ya ku Babiloni, wakonzekera kuti amenyane nanu,” akutero Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 “Thawani mofulumira! Kabisaleni mʼmakhwawa, inu anthu ku Hazori,” akutero Yehova. “Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni wakukonzerani chiwembu; wakonzekera zoti alimbane nanu.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 49:30
4 Mawu Ofanana  

Koma iye safuna chotero, ndipo mtima wake suganizira chotero, koma mtima wake ulikufuna kusakaza, ndi kuduladula amitundu osawerengeka.


taonani, Ine, ndidzatuma ndi kutenga mabanja onse a kumpoto, ati Yehova, ndipo ndidzatuma kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni, mtumiki wanga, ndipo ndidzatengera iwo padziko lino, ndi pa okhalamo ake onse, ndi pa mitundu iyi yozungulira, ndipo ndidzathetsa iwo ndithu, ndi kuwayesa iwo chizizwitso, ndi chotsonyetsa, ndi bwinja lamuyaya.


Tsopano ndapereka maiko onse awa m'manja a Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni, mtumiki wanga; ndiponso nyama zakuthengo ndampatsa iye kuti zimtumikire.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa