Yeremiya 49:2 - Buku Lopatulika2 Chifukwa chake, taonani, masiku afika, ati Yehova, Ine ndidzamveketsa mfuu ya nkhondo yomenyana ndi Raba wa ana a Amoni; ndipo adzasanduka muunda wabwinja, ndipo midzi yake idzatenthedwa ndi moto; pamenepo Israele adzalanda iwo amene adamlanda, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Chifukwa chake, taonani, masiku afika, ati Yehova, Ine ndidzamveketsa mfuu ya nkhondo yomenyana ndi Raba wa ana a Amoni; ndipo adzasanduka muunda wabwinja, ndipo ana ake akazi adzatenthedwa ndi moto; pamenepo Israele adzalanda iwo amene adamlanda, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndipotu nthaŵi ikudza, pamene ndidzamveketse mfuu wankhondo ku Raba, likulu la ku Amoni. Mzinda umenewo udzasanduka bwinja lopanda anthu, ndipo midzi yake idzapserera. Tsono Israele adzaŵalanda zao adaniwo amene adamulanda zake,” akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Koma nthawi ikubwera,” akutero Yehova, “pamene ndidzamveketse mfuwu wankhondo ku Raba, likulu la Amoni; ndipo malo awo opembedzera milungu yawo adzatenthedwa ndi moto. Choncho Aisraeli adzalandanso dziko lawo kuchokera kwa amene anawalanda poyamba dzikolo,” akutero Yehova. Onani mutuwo |