Yeremiya 49:14 - Buku Lopatulika14 Ndamva mthenga wa kwa Yehova, ndipo mthenga watumidwa mwa amitundu, wakuti, Sonkhanani, mumdzere, nimuukire nkhondo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndamva mthenga wa kwa Yehova, ndipo mthenga watumidwa mwa amitundu, wakuti, Sonkhanani, mumdzere, nimuukire nkhondo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ndamva uthenga wochokera kwa Chauta wamthenga watumidwa kwa anthu a mitundu ina. Akufuula kuti, “Sonkhanani pamodzi kuti mumenyane ndi Edomu, dzambatukani mukonzekere nkhondo! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndamva uthenga wochokera kwa Yehova: Nthumwi yatumidwa kupita kwa anthu a mitundu ina kukanena kuti, “Sonkhanani pamodzi kuti muthire nkhondo Edomu! Konzekerani nkhondo!” Onani mutuwo |