Yeremiya 48:47 - Buku Lopatulika47 Koma ndidzabwezanso undende wa Mowabu masiku akumaliza, ati Yehova. Ziweruzo za Mowabu ndi zomwezi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Koma ndidzabwezanso undende wa Mowabu masiku akumaliza, ati Yehova. Ziweruzo za Mowabu ndi zomwezi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Komabe masiku akutsogolo ndidzambwezeranso ufulu Mowabu,” akutero Chauta. Chiweruzo cha Mowabu chathera pamenepa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 “Komabe masiku akutsogolo ndidzabwezeranso Mowabu chuma chake,” akutero Yehova. Chiweruzo cha Mowabu chathera pamenepa. Onani mutuwo |