Yeremiya 48:44 - Buku Lopatulika44 Ndipo iye wakuthawa chifukwa cha mantha adzagwa m'dzenje; ndi iye amene atuluka m'dzenje adzagwidwa m'khwekhwe; pakuti ndidzatengera pa iye, pa Mowabu, chaka cha kulangidwa kwao, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Ndipo iye wakuthawa chifukwa cha mantha adzagwa m'dzenje; ndi iye amene atuluka m'dzenje adzagwidwa m'khwekhwe; pakuti ndidzatengera pa iye, pa Mowabu, chaka cha kulangidwa kwao, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 “Wothaŵa nkhaŵa, adzagwa m'dzenje. Wotuluka m'dzenje, adzakodwa mu msampha. Zimenezi nzimene ndidzamgwetsere Mowabu pa nthaŵi ya chilango chake,” akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 “Aliyense wothawa zoopsa adzagwera mʼdzenje, aliyense wotuluka mʼdzenje adzakodwa mu msampha. Ndigwetsa zimenezi pa Mowabu pa nthawi ya chilango chake,” akutero Yehova. Onani mutuwo |