Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 48:43 - Buku Lopatulika

43 Mantha, ndi dzenje, ndi khwekhwe, zili pa iwe, wokhala mu Mowabu, ati Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 Mantha, ndi dzenje, ndi khwekhwe, zili pa iwe, wokhala m'Mowabu, ati Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 Nkhaŵa, dzenje ndi msampha zikuyembekeza inu anthu okhala ku Mowabu,” akutero Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 Zoopsa, dzenje ndi msampha zikudikira inu anthu a ku Mowabu,” akutero Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 48:43
6 Mawu Ofanana  

Adzagwetsa pwatapwata misampha pa oipa; moto ndi miyala ya sulufure, ndi mphepo yoopsa zidzawagawikira m'chikho chao.


Taona ndidzakutengera mantha, ati Ambuye, Yehova wa makamu, akuchokera kwa onse amene akuzungulira iwe; ndipo mudzaingitsidwa yense kulozera maso ake, ndipo palibe amene adzasonkhanitsa osochera.


Ndakutchera iwe msampha, ndi iwenso wagwidwa, iwe Babiloni, ndipo sunadziwe, wapezeka, ndiponso wagwidwa, chifukwa walimbana ndi Yehova.


Mantha ndi dzenje zitifikira, ndi phokoso ndi chionongeko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa