Yeremiya 48:41 - Buku Lopatulika41 Keriyoti walandidwa, ndi malinga agwidwa, ndipo tsiku lomwelo mtima wa anthu amphamvu a Mowabu adzakhala ngati mtima wa mkazi alinkudwala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Keriyoti walandidwa, ndi malinga agwidwa, ndipo tsiku lomwelo mtima wa anthu amphamvu a Mowabu adzakhala ngati mtima wa mkazi alinkudwala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Mizinda idzagwidwa, malinga adzalandidwa. Tsiku limenelo mitima ya ankhondo a ku Mowabu idzakhala ili thithithi ndi mantha, ngati mkazi pa nthaŵi yake yochira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Mizinda idzagwidwa ndipo malinga adzalandidwa. Pa tsiku limenelo mitima ya ankhondo a ku Mowabu idzakhala ngati mtima wa mayi pa nthawi yake yochira. Onani mutuwo |