Yeremiya 48:40 - Buku Lopatulika40 Pakuti Yehova atero: Taonani, adzauluka ngati chiombankhanga, adzamtambasulira Mowabu mapiko ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Pakuti Yehova atero: Taonani, adzauluka ngati chiombankhanga, adzamtambasulira Mowabu mapiko ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Chauta akunena kuti, “Mtundu wina udzachita kuuluka nkudzagwera Mowabu ngati nkhwazi ya mapiko otambalitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Yehova akuti, “Mtundu wina udzachita kuwuluka nʼkugwera pa Mowabu ngati chiwombankhanga chimene chatambalitsa mapiko ake. Onani mutuwo |