Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 48:31 - Buku Lopatulika

31 Chifukwa chake ndidzakuwira Mowabu; inde, ndidzafuulira Mowabu yense, adzalirira anthu a ku Kiriheresi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Chifukwa chake ndidzakuwira Mowabu; inde, ndidzafuulira Mowabu yense, adzalirira anthu a ku Kiriheresi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Motero ndikulira chifukwa cha Mowabu. Ndikulira mwachisoni chifukwa cha anthu onse a ku Mowabu. Ndikulira anthu a ku Kiriheresi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Nʼchifukwa chake ndidzamulira Mowabu, ine ndikulira chifukwa cha anthu onse a ku Mowabu, ndikubuwula chifukwa cha anthu a ku Kiri Heresi.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 48:31
4 Mawu Ofanana  

Napasula mizinda, naponya yense mwala wake panthaka ponse pabwino, naidzaza, nafotsera zitsime zonse zamadzi, nagwetsa mitengo yonse yabwino, kufikira anasiya miyala yake mu Kiri-Haresefi mokha; koma oponya miyala anauzinga, naukantha.


Mtima wanga ufuula chifukwa cha Mowabu: akulu ake athawira ku Zowari, ku Egilati-Selisiya; pakuti pa chikweza cha Luhiti akwera alikulira, pakuti m'njira ya Horonaimu akweza mfuu wa chionongeko.


Chifukwa chake mtima wanga umlirira Mowabu monga zitoliro, ndipo mtima wanga uwalirira anthu a Kiriheresi monga zitoliro, chifukwa chake zakuchuluka zake adadzionera zatayika.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa