Yeremiya 48:30 - Buku Lopatulika30 Ine ndidziwa mkwiyo wake, ati Yehova, kuti uli chabe; zonyenga zake sizinachite kanthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ine ndidziwa mkwiyo wake, ati Yehova, kuti uli chabe; zonyenga zake sizinachita kanthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Ndikudziŵa kudzikuza kwake. Mau ake odzitama ngachabechabe, ntchito zake nzopanda pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Ine ndikuzidziwa ntchito zake, akutero Yehova. Ntchitozo ndi nʼzosapindulitsa kanthu. Onani mutuwo |