Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 48:23 - Buku Lopatulika

23 ndi pa Kiriyataimu, ndi pa Betegamuli, ndi pa Betemeoni;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 ndi pa Kiriyataimu, ndi pa Betegamuli, ndi pa Betemeoni;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Kiriyataimu, Betegamuli, Betemeoni,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Kiriyataimu, Beti-Gamuli, Beti-Meoni,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 48:23
7 Mawu Ofanana  

Chaka chakhumi ndi chinai ndipo anadza Kedorilaomere ndi mafumu amene anali naye, nawakantha Arefaimu mu Asiteroti-Karanaimu, ndi Azuzimu mu Hamu, ndi Aemimu mu Savekiriyataimu,


Za Mowabu. Atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele: Tsoka Nebo! Pakuti wapasuka; Kiriyataimu wachitidwa manyazi, wagwidwa; linga la pamtunda lachitidwa manyazi lapasudwa.


ndi pa Diboni, ndi pa Nebo, ndi pa Betedibilataimu;


chifukwa chake taona ndidzatsegula pambali pake pa Mowabu kuyambira kumizinda, kumizinda yake yokhala mphepete, yokometsetsa ya m'dziko, Beteyesimoti, Baala-Meoni, ndi Kiriyataimu,


ndi Nebo, ndi Baala-Meoni (anasintha maina ao), ndi Sibima; ndipo anaitcha mizinda adaimanga ndi maina ena.


Hesiboni ndi mizinda yake yonse yokhala pachidikha; Diboni, ndi Bamoti-Baala ndi Bete-Baala-Meoni;


ndi Kiriyataimu, ndi Sibima, ndi Zeretisahara, m'phiri la kuchigwa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa