Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 48:22 - Buku Lopatulika

22 ndi pa Diboni, ndi pa Nebo, ndi pa Betedibilataimu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 ndi pa Diboni, ndi pa Nebo, ndi pa Betedibilataimu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 ndi Diboni, Nebo ndi Betedibilataimu,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Diboni, Nebo, Beti-Dibilataimu,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 48:22
9 Mawu Ofanana  

Akwera ku Kachisi, ndi ku Diboni, kumisanje, kukalira; pa Nebo ndi pa Medeba a Mowabu pali kulira; pamitu pao ponse pali dazi, ndevu zonse zametedwa.


Za Mowabu. Atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele: Tsoka Nebo! Pakuti wapasuka; Kiriyataimu wachitidwa manyazi, wagwidwa; linga la pamtunda lachitidwa manyazi lapasudwa.


Iwe mwana wamkazi wokhala mu Diboni, utsike pa ulemerero wako, nukhale ndi ludzu; pakuti wakufunkha Mowabu wakukwerera, iwe waononga malinga ako.


Chiweruzo chafika padziko lachidikha; pa Holoni, ndi pa Yahazi, ndi pa Mefaati;


ndi pa Kiriyataimu, ndi pa Betegamuli, ndi pa Betemeoni;


Ndipo ndidzawatambasulira dzanja langa, ndi kulisandutsa dziko bwinja ndi lopasuka, koposa chipululu cha ku Ribula mokhalamo iwo monse; ndipo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.


Tinawagwetsa; Hesiboni waonongeka kufikira ku Diboni, ndipo tinawapululutsa kufikira ku Nofa. Ndiwo wakufikira ku Medeba.


Ndipo ana a Gadi anamanga Diboni, ndi Ataroti, ndi Aroere;


Nachokera ku Diboni Gadi, nayenda namanga mu Alimoni-Dibulataimu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa