Yeremiya 48:20 - Buku Lopatulika20 Mowabu wachitidwa manyazi, pakuti wathyoka; kuwa nulire, nunene mu Arinoni, kuti Mowabu wapasuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Mowabu wachitidwa manyazi, pakuti wathyoka; kuwa nulire, nunene m'Arinoni, kuti Mowabu wapasuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Iwo adzayankha kuti, ‘Ukutu Mowabu wagwa, amchititsa manyazi, mlireni mofuula. Mulengeze ku mtsinje wa Arinoni kuti Mowabu wasanduka bwinja.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iwo adzayankha kuti, “Mowabu wachititsidwa manyazi, pakuti wasakazika. Lirani mwachisoni ndipo fuwulani! Lengezani ku mtsinje wa Arinoni kuti Mowabu wawonongedwa. Onani mutuwo |