Yeremiya 48:18 - Buku Lopatulika18 Iwe mwana wamkazi wokhala mu Diboni, utsike pa ulemerero wako, nukhale ndi ludzu; pakuti wakufunkha Mowabu wakukwerera, iwe waononga malinga ako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Iwe mwana wamkazi wokhala m'Diboni, utsike pa ulemerero wako, nukhale ndi ludzu; pakuti wakufunkha Mowabu wakukwerera, iwe waononga malinga ako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 “Inu anthu a ku Diboni, tsikanipo pa ulemerero wanu, khalani pansi poumapa. Woononga Mowabu wafika kudzamenyana nanu, wapasula malinga anu ankhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 “Tsikani pa ulemerero wanu ndipo khalani pansi powuma, inu anthu okhala ku Diboni, pakuti wowononga Mowabu wabwera kudzamenyana nanu, wasakaza mizinda yanu yotetezedwa. Onani mutuwo |