Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 48:17 - Buku Lopatulika

17 Inu nonse akumzungulira, mumchitire iye chisoni, inu nonse akudziwa dzina lake; muti, Chibonga cholimba chathyokatu, ndodo yokoma!

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Inu nonse akumzungulira, mumchitire iye chisoni, inu nonse akudziwa dzina lake; muti, Chibonga cholimba chathyokatu, ndodo yokoma!

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Mumvereni chisoni kwambiri inu nonse anansi ake, anzake nonse amene mumamdziŵa. Ndipo munene kuti, ‘Ogo, taonani m'mene yathyokera ndodo yachifumu yamphamvu ija! Taonani m'mene yathyokera ndodo yaulemu ija!’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Mulireni kwambiri, inu nonse amene mwamuzungulira, inu nonse amene mumadziwa za kutchuka kwake; nenani kuti, “Taonani momwe yathyokera ndodo yamphamvu yaufumu ija, taonani momwe ndodo yaulemu yathyokera!”

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 48:17
12 Mawu Ofanana  

Yehova adzatumiza ndodo ya mphamvu yanu kuchokera ku Ziyoni; chitani ufumu pakati pa adani anu.


Iwe Asiriya chibonga cha mkwiyo wanga, ndodo m'dzanja lake muli ukali wanga!


Wokantha anthu mwaukali kuwakantha chikanthire, wolamulira amitundu mokwiya, angosautsidwa wopanda womlanditsa.


Pakuti minda ya ku Hesiboni yalefuka, ndi mpesa wa ku Sibima; ambuye a mitundu athyolathyola mitengo yosankhika yake; iwo anafikira ngakhale ku Yazere, nayendayenda m'chipululu; nthambi zake zinatasa, zinapitirira panyanja.


Pakuti goli la katundu wake, ndi mkunkhu wa paphewa pake, ndodo ya womsautsa, inu mwazithyola monga tsiku la Midiyani.


Yasweka bwanji! Akuwa bwanji Mowabu! Wapotoloka bwanji ndi manyazi! Chomwecho Mowabu adzakhala choseketsa ndi choopsera onse omzungilira iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa