Yeremiya 48:16 - Buku Lopatulika16 Tsoka la Mowabu layandikira kudza, nsautso yake ifulumiratu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Tsoka la Mowabu layandikira kudza, nsautso yake ifulumiratu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Kugwa kwa Mowabu kuli pafupi. Chiwonongeko changokhala pang'onong'ono kuti chimugwere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kugwa kwa Mowabu kuli pafupi; masautso ake akubwera posachedwa. Onani mutuwo |