Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 48:16 - Buku Lopatulika

16 Tsoka la Mowabu layandikira kudza, nsautso yake ifulumiratu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Tsoka la Mowabu layandikira kudza, nsautso yake ifulumiratu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Kugwa kwa Mowabu kuli pafupi. Chiwonongeko changokhala pang'onong'ono kuti chimugwere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Kugwa kwa Mowabu kuli pafupi; masautso ake akubwera posachedwa.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 48:16
8 Mawu Ofanana  

mpaka muvi ukapyoza mphafa yake; amtsata monga mbalame yothamangira msampha; osadziwa kuti adzaononga moyo wake.


Ndipo mimbulu idzalira m'maboma ao, ndi ankhandwe m'manyumba ao abwino; ndi nthawi yake iyandikira, ndi masiku ake sadzachuluka.


Ndipo Yehova anati kwa ine, Waona bwino pakuti Ine ndidzadikira mau anga kuwachita.


Chifukwa chake unene nao, Atero Yehova Mulungu, Ndidzaleketsa mwambi uwu, ndipo sadzautchulanso mwambi mu Israele; koma unene nao, Masiku ayandikira, nadzachitika masomphenya ali onse.


Chifukwa chake uziti nao, Atero Ambuye Yehova, Palibe amodzi a mau anga adzazengerezekanso; koma mau ndidzanenawo adzachitika, ati Ambuye Yehova.


Kubwezera chilango nkwanga, kubwezera komwe, pa nyengo ya kuterereka phazi lao; pakuti tsiku la tsoka lao layandika, ndi zinthu zowakonzeratu zifulumira kudza.


Ndipo m'chisiriro adzakuyesani malonda ndi mau onyenga; amene chiweruzo chao sichinachedwe ndi kale lomwe, ndipo chitayiko chao sichiodzera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa