Yeremiya 48:14 - Buku Lopatulika14 Muti bwanji, Tili amphamvu, olimba mtima ankhondo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Muti bwanji, Tili amphamvu, olimba mtima ankhondo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Kodi mungathe kunena bwanji kuti, ‘Ife ndife ngwazi, asilikali olimba mtima pa nkhondo?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Kodi munganene bwanji kuti, ‘Ife ndife asilikali. Ife ndife ngwazi, anthu amphamvu pa nkhondo?’ Onani mutuwo |