Yeremiya 48:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Mowabu adzachita manyazi chifukwa cha Kemosi, monga nyumba ya Israele inachita manyazi chifukwa cha Betele amene anamkhulupirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Mowabu adzachita manyazi chifukwa cha Kemosi, monga nyumba ya Israele inachita manyazi chifukwa cha Betele amene anamkhulupirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Motero Mowabu adzachita manyazi ndi Kemosi, mulungu wake, monga momwe Israele adachitira naye manyazi Betele, mulungu amene ankamukhulupirira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pamenepo Mowabu adzachita manyazi ndi Kemosi, monga momwe Aisraeli anachitira manyazi ndi Beteli amene ankamukhutulira. Onani mutuwo |