Yeremiya 48:11 - Buku Lopatulika11 Mowabu wakhala m'mtendere kuyambira ubwana wake, wakhala pansenga, osatetekulidwa, sananke kundende; chifukwa chake makoleredwe ake alimobe mwa iye, fungo lake silinasinthike. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Mowabu wakhala m'mtendere kuyambira ubwana wake, wakhala pansenga, osatetekulidwa, sananke kundende; chifukwa chake makoleredwe ake alimobe mwa iye, fungo lake silinasinthika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mowabu wakhala pa mtendere kuyambira unyamata wake, ngati vinyo wokhazikika pa masese ake, osapungulidwa kuchoka mu mtsuko wina kuthira mu mtsuko wina. Sadatengedwe ukapolo. Nchifukwa chake khalidwe lake lili losasinthika, ndipo fungo lake lili lomwe lija.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Mowabu wakhala pa mtendere kuyambira ubwana wake, ngati vinyo wokhazikika pa masese ake, osapungulidwa kuchoka mu mtsuko wina kuthira mu mtsuko wina; iye sanatengedwepo ukapolo. Nʼchifukwa chake kukoma kwake nʼkomwe kuja ndipo fungo lake silinasinthe. Onani mutuwo |