Yeremiya 48:10 - Buku Lopatulika10 Atembereredwe iye amene agwira ntchito ya Yehova monyenga, atembereredwe iye amene abweza lupanga lake kumwazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Atembereredwe iye amene agwira ntchito ya Yehova monyenga, atembereredwe iye amene abweza lupanga lake kumwazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Ndi wotembereredwa amene amagwira ntchito ya Chauta mwaulesi. Ndi wotembereredwa amene amaletsa lupanga lake kutema ndi kupha anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Wotembereredwa munthu amene amagwira ntchito ya Yehova monyinyirika! Wotembereredwa munthu amene amaletsa lupanga lake kupha anthu! Onani mutuwo |