Yeremiya 47:2 - Buku Lopatulika2 Yehova atero: Taonani, madzi adzakwera kutuluka kumpoto, nadzakhala mtsinje wosefuka, nadzasefukira padziko ndi pa zonse zili m'mwemo, pamzinda ndi pa onse okhalamo; ndipo amuna adzalira, ndi onse okhala m'dziko adzakuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Yehova atero: Taonani, madzi adzakwera kutuluka kumpoto, nadzakhala mtsinje wosefuka, nadzasefukira padziko ndi pa zonse zili m'mwemo, pamudzi ndi pa onse okhalamo; ndipo amuna adzalira, ndi onse okhala m'dziko adzakuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adati, “Onani m'mene madzi akubwerera kuchokera kumpoto, adzakhala mtsinje wosefukira ndi wamkokomo. Adzasefukira m'dzikomo ndi kumiza zonse zokhala m'menemo, mizinda yonse, ndi anthu onse okhalamo. Anthu azidzafuula, onse okhala m'dzikomo azidzalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yehova akuti, “Taonani mmene madzi akubwerera kuchokera kumpoto; adzasanduka mtsinje wosefukira ndi a mkokomo. Adzasefukira mʼdziko monse ndi kumiza chilichonse mʼmenemo, mizinda ndi onse okhala mʼmenemo. Anthu adzafuwula; anthu onse okhala mʼdzikomo adzalira Onani mutuwo |