Yeremiya 47:1 - Buku Lopatulika1 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya mneneri onena za Afilisti, Farao asanakanthe Gaza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya mneneri onena za Afilisti, Farao asanakanthe Gaza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Naŵa mau amene Chauta adalankhula ndi mneneri Yeremiya, onena za Afilisti, Farao asanaononge Gaza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Uthenga umene Yehova anamupatsa mneneri Yeremiya wonena za Afilisti, Farao asanathire nkhondo Gaza ndi uwu: Onani mutuwo |