Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 46:3 - Buku Lopatulika

3 Konzani chikopa ndi lihawo, nimuyandikire kunkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Konzani chikopa ndi lihawo, nimuyandikire kunkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 “Konzani zishango ndi malihawo, yambanipo wa ku nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 anati, “Konzani zishango zanu ndi malihawo, ndipo yambanipo kupita ku nkhondo!

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 46:3
7 Mawu Ofanana  

Iwo akonza pa gome lodyera, aika alonda, adya, namwa; ukani, akalonga inu, dzozani mafuta chikopa.


Nenani mu Ejipito, lalikirani mu Migidoli, lalikirani mu Nofi ndi Tapanesi; nimuti, Udziimike, nudzikonzere wekha; pakuti lupanga ladya pozungulira pako.


Mulalikire ichi mwa amitundu, mukonzeretu nkhondo; utsani amuna amphamvu; amuna onse a nkhondo ayandikire nakwere.


Wophwanyayo wakwera pamaso pako; sunga linga, yang'anira panjira, limbitsa m'chuuno mwako, limbikitsatu mphamvu yako.


Udzitungiretu madzi a nthawi yokumangira misasa, limbikitsa malinga ako, lowa kuthope, ponda dothi, limbitsa ng'anjo yanjerwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa