Yeremiya 46:3 - Buku Lopatulika3 Konzani chikopa ndi lihawo, nimuyandikire kunkhondo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Konzani chikopa ndi lihawo, nimuyandikire kunkhondo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 “Konzani zishango ndi malihawo, yambanipo wa ku nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 anati, “Konzani zishango zanu ndi malihawo, ndipo yambanipo kupita ku nkhondo! Onani mutuwo |