Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 46:1 - Buku Lopatulika

1 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya mneneri akunena za amitundu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya mneneri akunena za amitundu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adauza mneneri Yeremiya mau onena za anthu a mitundu ina.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehova anamupatsa Yeremiya uthenga wonena za anthu a mitundu ina.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 46:1
13 Mawu Ofanana  

Amenewo ndipo anagawa zisumbu za amitundu m'maiko mwao, onse amene monga mwa chinenedwe chao; ndi mwa mabanja ao, ndi m'mitundu yao.


penyatu, lero ndakuika ulamulire mitundu ya anthu ndi maufumu, kuti uzule, upasule, uononge, ugwetse, umange, ubzale.


Mkango wakwera kutuluka m'nkhalango mwake, ndipo waononga amitundu ali panjira, watuluka m'mbuto mwake kuti achititse dziko lako bwinja, kuti mizinda yako ipasuke mulibenso wokhalamo.


Ndipo iye adzafika, nadzakantha dziko la Ejipito; nadzapereka kuimfa iwo a kuimfa, ndi kundende iwo a kundende, ndi kulupanga iwo a kulupanga.


Chaka chakhumi, mwezi wakhumi, tsiku lakhumi ndi chiwiri la mweziwo, anandidzera mau a Yehova, akuti,


Anandidzeranso mau a Yehova, akuti,


Ndipo kunali chaka chakhumi ndi chimodzi, mwezi wachitatu, tsiku loyamba la mwezi, anandidzera mau a Yehova, akuti,


Ndipo kunali chaka chakhumi ndi chiwiri, mwezi wakhumi ndi chiwiri, tsiku loyamba la mwezi, anandidzera mau a Yehova, akuti,


Kodi m'mwemo adzakhuthula mu ukonde mwake osaleka kuphabe amitundu?


Pakuti atero Yehova wa makamu: Utatha ulemererowo ananditumiza kwa amitundu amene anakufunkhani; pakuti iye wokhudza inu, akhudza mwana wa m'diso lake.


Pakuti, pokhala pamwamba pa matanthwe ndimpenya, pokhala pa zitunda ndimuyang'ana; taonani, ndiwo anthu akukhala pa okha. Osadziwerengera pakati pa amitundu ena.


Kapena Mulungu ndiye wa Ayuda okhaokha kodi? Si wao wa amitundunso kodi? Eya, wa amitundunso:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa