Yeremiya 46:1 - Buku Lopatulika1 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya mneneri akunena za amitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya mneneri akunena za amitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta adauza mneneri Yeremiya mau onena za anthu a mitundu ina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova anamupatsa Yeremiya uthenga wonena za anthu a mitundu ina. Onani mutuwo |