Yeremiya 45:4 - Buku Lopatulika4 Uzitero naye, Yehova atero: Taonani, chimene ndamanga ndidzapasula, ndi chimene ndaoka ndidzazula; ndidzatero m'dziko lonseli. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Uzitero naye, Yehova atero: Taonani, chimene ndamanga ndidzapasula, ndi chimene ndaoka ndidzazula; ndidzatero m'dziko lonseli. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta adandiwuza kuti ndilankhule mau aŵa kwa iwe Baruki, ‘Chimene ndidamanga, ndikuchigwetsa. Chimene ndidabzala, ndikuchizula. Umu ndi m'mene ndidzachitire ndi dziko lonse lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Koma Yehova akukuwuza kuti, “Ndidzagwetsa chimene ndinamanga ndipo ndidzazula chimene ndinadzala. Ndidzachita zimenezi mʼdziko lonse. Onani mutuwo |