Yeremiya 44:3 - Buku Lopatulika3 chifukwa cha choipa chao anachichita kuutsa nacho mkwiyo wanga; pakuti anapita kukafukizira, ndi kutumikira milungu ina, imene sanaidziwe, ngakhale iwo, ngakhale inu, ngakhale makolo anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 chifukwa cha choipa chao anachichita kuutsa nacho mkwiyo wanga; pakuti anapita kukafukizira, ndi kutumikira milungu ina, imene sanaidziwe, ngakhale iwo, ngakhale inu, ngakhale makolo anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Zonsezi zidachitika chifukwa cha machimo a anthu amene adaputa mkwiyo wanga, pofukizira lubani milungu ina ndi kumaitumikira, milungu imene sadaidziŵe iwowo kapena inu kapenanso makolo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Zimenezi zinachitika chifukwa cha zoyipa zomwe anachita. Iwo anaputa mkwiyo wanga pofukiza lubani ndi potumikira milungu ina imene iwo kapena inu ngakhalenso makolo anu sanayidziwe. Onani mutuwo |