Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 43:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo anafika mau a Yehova kwa Yeremiya mu Tapanesi, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo anafika mau a Yehova kwa Yeremiya m'Tapanesi, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Chauta adalankhula ndi Yeremiya ku Tapanesi. Adamuuza kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ndipo Yehova anayankhula ndi Yeremiya ku Tapanesi kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 43:8
11 Mawu Ofanana  

Ndidzapita kuti kuzembera mzimu wanu? Kapena ndidzathawira kuti kuzembera nkhope yanu?


Ananso a Nofi ndi a Tapanesi, anaswa pakati pamutu pako.


Tenga miyala yaikulu m'dzanja lako, nuiyale ndi dothi pakati pa njerwa, za pa khomo la nyumba ya Farao mu Tapanesi pamaso pa anthu a Yuda;


Mau amene anadza kwa Yeremiya onena za Ayuda onse amene anakhala m'dziko la Ejipito, okhala pa Migidoli, ndi pa Tapanesi, ndi pa Nofi, ndi m'dziko la Patirosi, akuti,


Nenani mu Ejipito, lalikirani mu Migidoli, lalikirani mu Nofi ndi Tapanesi; nimuti, Udziimike, nudzikonzere wekha; pakuti lupanga ladya pozungulira pako.


Chaka chakhumi, mwezi wakhumi, tsiku lakhumi ndi chiwiri la mweziwo, anandidzera mau a Yehova, akuti,


Anandidzeranso mau a Yehova, akuti,


Ndi ku Tehafinehesi kudzada usana, pakuthyola Ine magoli a Ejipito komweko; ndi mphamvu yake yodzikuza idzalekeka m'menemo; kunena za ilo mtambo udzaliphimba, ndi ana ake aakazi adzalowa undende.


Ndipo kunali chaka chakhumi ndi chimodzi, mwezi wachitatu, tsiku loyamba la mwezi, anandidzera mau a Yehova, akuti,


Ndipo kunali chaka chakhumi ndi chiwiri, mwezi wakhumi ndi chiwiri, tsiku loyamba la mwezi, anandidzera mau a Yehova, akuti,


m'menemo ndimva zowawa kufikira zomangira, monga wochita zoipa; koma mau a Mulungu samangika.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa