Yeremiya 43:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo anafika mau a Yehova kwa Yeremiya mu Tapanesi, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo anafika mau a Yehova kwa Yeremiya m'Tapanesi, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chauta adalankhula ndi Yeremiya ku Tapanesi. Adamuuza kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndipo Yehova anayankhula ndi Yeremiya ku Tapanesi kuti, Onani mutuwo |