Yeremiya 43:7 - Buku Lopatulika7 ndipo anadza nalowa m'dziko la Ejipito; pakuti sanamvere mau a Yehova; ndipo anadza mpaka ku Tapanesi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 ndipo anadza nalowa m'dziko la Ejipito; pakuti sanamvere mau a Yehova; ndipo anadza mpaka ku Tapanesi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Onsewo adapita nawo ku Ejipito monyoza mau a Chauta, nakafika ku Tapanesi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Kotero anthuwo analowa mʼdziko la Igupto chifukwa anakana kumvera Yehova, nakafika ku Tapanesi. Onani mutuwo |