Yeremiya 43:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Yohanani mwana wake wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo, ndi anthu onse sanamvere mau a Yehova, kuti akhale m'dziko la Yuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Yohanani mwana wake wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo, ndi anthu onse sanamvere mau a Yehova, kuti akhale m'dziko la Yuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri onse a ankhondo, pamodzi ndi anthu onse a ku Yuda, adakana kumvera Chauta ndipo sadakhale ku Yuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Motero Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri onse a ankhondo pamodzi ndi anthu onse sanamvere lamulo la Yehova loti akhale mʼdziko la Yuda. Onani mutuwo |