Yeremiya 43:3 - Buku Lopatulika3 koma Baruki mwana wake wa Neriya atisonkhezera zoipa za inu, mutipereke m'dzanja la Ababiloni, kuti atiphe ife, atitengere ife am'nsinga ku Babiloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 koma Baruki mwana wake wa Neriya atichichizira inu, mutipereke m'dzanja la Ababiloni, kuti atiphe ife, atitengere ife am'nsinga ku Babiloni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Baruki mwana wa Neriya ndiye wakukakamiza kuti utiletse, ndipo kuti tigwe m'manja mwa Ababiloni, kuti atiphe kapena kutitenga ukapolo kupita ku Babiloni.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Koma ndi Baruki mwana wa Neriya amene akukulimbikitsa kuti utiletse zopita ku Igupto ndi kuti mʼmalo mwake tidzipereke mʼmanja mwa Ababuloni, kuti iwo atiphe kapena kutitenga ukapolo ku Babuloni.” Onani mutuwo |