Yeremiya 43:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo panali pamene Yeremiya anatha kunena kwa anthu onse mau onse a Yehova Mulungu wao, amene anamtuma iye nao Yehova Mulungu wao, mau onse amenewo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo panali pamene Yeremiya anatha kunena kwa anthu onse mau onse a Yehova Mulungu wao, amene anamtuma iye nao Yehova Mulungu wao, mau onse amenewo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yeremiya atatsiriza kuuza anthu zonse zimene Chauta Mulungu wao adamtuma kuti akaŵauze, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yeremiya atatsiriza kuwawuza anthuwo mawu onse a Yehova Mulungu wawo, amene Yehova anamutuma kuti akawawuze, Onani mutuwo |