Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 42:9 - Buku Lopatulika

9 nati kwa iwo, Atero Yehova, Mulungu wa Israele, kwa Iye amene munandituma ine ndigwetse pembedzero lanu pamaso pake,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 nati kwa iwo, Atero Yehova, Mulungu wa Israele, kwa Iye amene munandituma ine ndigwetse pembedzero lanu pamaso pake,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Adaŵauza kuti, “Chauta, Mulungu wa Israele, amene mudaandituma kuti ndikampemphe kanthu m'dzina lanu, akunena kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Yehova, Mulungu wa Israeli amene munanditumako kuti ndikapereke madandawulo mʼdzina lanu akuti,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 42:9
6 Mawu Ofanana  

Kapena Yehova Mulungu wanu adzamva mau onse a kazembeyo, amene anamtuma mfumu ya Asiriya mbuye wake, kuti atonze Mulungu wamoyo, nadzamlanga chifukwa cha mau adawamva Yehova Mulungu wanu; chifukwa chake uwakwezere otsalawo pemphero.


Nanena nao Yesaya, Muzitero kwa mbuye wanu, Atero Yehova, Musamaopa mau mudawamva, amene anyamata a mfumu ya Asiriya anandichitira nao mwano.


nati kwa Yeremiya mneneri, Chipembedzero chathu chigwe pamaso panu, nimutipempherere ife kwa Yehova Mulungu wanu, chifukwa cha otsala onsewa; pakuti tatsala ife owerengeka m'malo mwa ambiri, monga maso anu ationa ife;


Ndipo anaitana Yohanani mwana wake wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala naye, ndi anthu onse kuyambira wamng'ono kufikira wamkulu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa