Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 42:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo anaitana Yohanani mwana wake wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala naye, ndi anthu onse kuyambira wamng'ono kufikira wamkulu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo anaitana Yohanani mwana wake wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala naye, ndi anthu onse kuyambira wamng'ono kufikira wamkulu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Tsono Yeremiya adaitana Yohanani mwana wa Kareya, pamodzi ndi atsogoleri onse a ankhondo amene anali nawo, ndiponso anthu onse, ang'onoang'ono ndi akuluakulu omwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Choncho Yeremiya anayitana Yohanani mwana wa Kareya pamodzi ndi atsogoleri onse a ankhondo amene anali naye ndiponso anthu onse, ana ndi akulu omwe.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 42:8
7 Mawu Ofanana  

Ndiponso Yohanani mwana wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala m'minda, anadza kwa Gedaliya ku Mizipa,


pamenepo anadza kwa Gedaliya ku Mizipa, Ismaele mwana wa Netaniya, ndi Yohanani ndi Yonatani ana a Kareya, ndi Seraya mwana wa Tanumeti, ndi ana a Efayi wa ku Netofa, ndi Yezaniya mwana wa munthu wa ku Maaka, iwo ndi anthu ao.


Ndipo akazembe onse a nkhondo, ndi Yohanani mwana wake wa Kareya, ndi Yezaniya mwana wake wa Hosaya, ndi anthu onse kuyambira wamng'ono, kufikira wamkulu, anayandikira,


Ndipo panali atapita masiku khumi, mau a Yehova anadza kwa Yeremiya.


nati kwa iwo, Atero Yehova, Mulungu wa Israele, kwa Iye amene munandituma ine ndigwetse pembedzero lanu pamaso pake,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa