Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 42:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo panali atapita masiku khumi, mau a Yehova anadza kwa Yeremiya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo panali atapita masiku khumi, mau a Yehova anadza kwa Yeremiya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Atatha masiku khumi, Chauta adalankhula ndi Yeremiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Patapita masiku khumi, Yehova anayankhula ndi Yeremiya.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 42:7
7 Mawu Ofanana  

Yembekeza Yehova, limbika, ndipo Iye adzalimbitsa mtima wako; inde, yembekeza Yehova.


chifukwa chake Ambuye Yehova atero, Taonani, ndiika mu Ziyoni mwala wa maziko, mwala woyesedwa mwala wa pangodya, wa mtengo wake wokhazikika ndithu; wokhulupirira sadzafulumira.


Chifukwa chake Yehova adzadikira, kuti akukomereni mtima, ndipo chifukwa chake Iye adzakuzidwa, kuti akuchitireni inu chifundo; pakuti Yehova ndiye Mulungu wa chiweruziro; odala ali onse amene amdikira Iye.


Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, Nebuzaradani kapitao wa alonda atammasula pa Rama, pamene anamtenga iye womangidwa m'maunyolo pamodzi ndi am'nsinga onse a Yerusalemu ndi Yuda, amene anatengedwa am'nsinga kunka nao ku Babiloni.


Ndipo anaitana Yohanani mwana wake wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala naye, ndi anthu onse kuyambira wamng'ono kufikira wamkulu,


Ndipo kunali atatha masiku asanu ndi awiri, mau a Yehova anandidzera, ndi kuti,


Pakuti masomphenyawo alindira nyengo yoikidwiratu, ndipo afulumirira potsirizira pake, osanama; akachedwa uwalindirire; popeza afika ndithu, osazengereza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa