Yeremiya 42:16 - Buku Lopatulika16 pamenepo padzakhala, kuti lupanga limene muopa lidzakupezani m'menemo m'dziko la Ejipito, ndi njala, imene muiopa, idzakuumirirani kumeneko ku Ejipito; pamenepo mudzafa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 pamenepo padzakhala, kuti lupanga limene muopa lidzakupezani m'menemo m'dziko la Ejipito, ndi njala, imene muiopa, idzakuumirirani kumeneko ku Ejipito; pamenepo mudzafa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 ndiye kuti nkhondo mukuiwopayo idzakugonjetsani ku Ejipito komweko. Njala mukuiwopayo idzakuvutanibe ngakhale ku Ejipitoko, ndipo mudzafera kumeneko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 ndiye nkhondo imene mukuyiopayo idzakugonjetsani ku Igupto komweko. Njala imene mukuyiopayo idzakupezani ku Igupto komweko ndipo mudzafera kumeneko. Onani mutuwo |