Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 42:13 - Buku Lopatulika

13 Koma mukati, Sitidzakhala m'dziko muno; osamvera mau a Yehova Mulungu wanu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Koma mukati, Sitidzakhala m'dziko muno; osamvera mau a Yehova Mulungu wanu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Koma mwina simumvera mau a Chauta, nkunena kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 “Koma mwina simudzamvera Yehova Mulungu wanu nʼkumanena kuti, ‘Ayi ife sitidzakhala mʼdziko muno,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 42:13
3 Mawu Ofanana  

Koma Farao anati, Yehova ndani, kuti ndimvere mau ake ndi kulola Israele apite? Sindimdziwa Yehova, ndiponso sindidzalola Israele apite.


Ngati mudzakhalabe m'dziko muno, ndidzamangitsa mudzi wanu, osakugumulani, ndidzakuokani inu, osakuzulani; pakuti ndagwidwa nacho chisoni choipa chimene ndakuchitirani inu.


Koma mau amene wanena ndi ife m'dzina la Yehova, sitidzakumvera iwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa