Yeremiya 42:13 - Buku Lopatulika13 Koma mukati, Sitidzakhala m'dziko muno; osamvera mau a Yehova Mulungu wanu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma mukati, Sitidzakhala m'dziko muno; osamvera mau a Yehova Mulungu wanu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma mwina simumvera mau a Chauta, nkunena kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 “Koma mwina simudzamvera Yehova Mulungu wanu nʼkumanena kuti, ‘Ayi ife sitidzakhala mʼdziko muno, Onani mutuwo |