Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 42:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo ndidzakuchitirani inu chifundo, kuti iye akuchitireni inu chifundo, nakubwezereni inu kudziko lanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo ndidzakuchitirani inu chifundo, kuti iye akuchitireni inu chifundo, nakubwezereni inu kudziko lanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Ndidzakuchitirani chifundo, kotero kuti iyenso adzakuchitirani chifundo ndi kukulolani kuti mukhale m'dziko lanu lino.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ndidzakuchitirani chifundo, ndipo mfumuyonso idzakuchitirani chifundo ndi kukulolani kuti mukhale mʼdziko mwanumwanu.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 42:12
3 Mawu Ofanana  

Ambuye, mutcherere khutu pemphero la kapolo wanu, ndi pemphero la akapolo anu okondwera nako kuopa dzina lanu; ndipo mupambanitse kapolo wanu lero lino, ndi kumuonetsera chifundo pamaso pa munthu uyu. Koma ndinali ine wothirira mfumu chakumwa chake.


Njira za munthu zikakonda Yehova ayanjanitsana naye ngakhale adani ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa