Yeremiya 42:10 - Buku Lopatulika10 Ngati mudzakhalabe m'dziko muno, ndidzamangitsa mudzi wanu, osakugumulani, ndidzakuokani inu, osakuzulani; pakuti ndagwidwa nacho chisoni choipa chimene ndakuchitirani inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ngati mudzakhalabe m'dziko muno, ndidzamangitsa mudzi wanu, osakugumulani, ndidzakuokani inu, osakuzulani; pakuti ndagwidwa nacho chisoni choipa chimene ndakuchitirani inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 ‘Ngati mukhala m'dziko lino, ndiye kuti mudzakhazikika, sindidzakuchotsani. Zoonadi, ndidzakukhazikitsani, osakuchotsani konse. Ndikumva chisoni chifukwa cha mazunzo amene ndidagwetsa pa inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Ngati mukhala mʼdziko muno, ndiye kuti ndidzakukhazikitsani, osakuchotsani. Inde ndidzakudzalani osakuchotsani pakuti ndi kumva chisoni kwambiri chifukwa cha mavuto amene ndabweretsa pa inu. Onani mutuwo |