Yeremiya 41:18 - Buku Lopatulika18 chifukwa cha Ababiloni; pakuti anawaopa, chifukwa Ismaele mwana wake wa Netaniya anapha Gedaliya mwana wake wa Ahikamu, amene mfumu ya ku Babiloni anamuika wolamulira m'dzikomo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 chifukwa cha Ababiloni; pakuti anawaopa, chifukwa Ismaele mwana wake wa Netaniya anapha Gedaliya mwana wake wa Ahikamu, amene mfumu ya ku Babiloni anamuika wolamulira m'dzikomo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 chifukwa choopa Ababiloni. Anali ndi manthadi chifukwa choti Ismaele mwana wa Netaniya, adaapha Gedaliya, mwana wa Ahikamu, amene mfumu ya ku Babiloni idaamuika kuti akhale bwanamkubwa wa dziko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 kuthawa Ababuloni. Iwo anaopa Ababuloniwo chifukwa Ismaeli mwana wa Netaniya anapha Gedaliya mwana wa Ahikamu, amene mfumu ya ku Babuloni inamuyika kukhala bwanamkubwa wa dzikolo. Onani mutuwo |