Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 41:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo anthu onse amene Ismaele anatenga ndende kuwachotsa mu Mizipa anatembenuka nabwera, nanka kwa Yohanani mwana wake wa Kareya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo anthu onse amene Ismaele anatenga ndende kuwachotsa m'Mizipa anatembenuka nabwera, nanka kwa Yohanani mwana wake wa Kareya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Anthu onse amene Ismaele adaaŵatenga ukapolo kuchoka nawo ku Mizipa, adabwerera napita kwa Yohanani mwana wa Kareya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Anthu onse amene Ismaeli anawagwira ukapolo ku Mizipa anabwerera ndi kupita kwa Yohanani mwana wa Kareya.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 41:14
3 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene anthu onse amene anali ndi Ismaele anaona Yohanani mwana wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala naye, anasekera.


Koma Ismaele mwana wake wa Netaniya anapulumuka Yohanani ndi anthu asanu ndi atatu, nanka kwa ana a Amoni.


kwa Akanani kum'mawa ndi kumadzulo, ndi kwa Aamori ndi Ahiti, ndi Aperizi ndi Ayebusi kumapiri, ndi kwa Ahivi kunsi kwa Heremoni, m'dziko la Mizipa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa