Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 41:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo panali pamene anthu onse amene anali ndi Ismaele anaona Yohanani mwana wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala naye, anasekera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo panali pamene anthu onse amene anali ndi Ismaele anaona Yohanani mwana wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala naye, anasekera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Ndipo anthu onse amene Ismaele adaaŵagwira ataona Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri a magulu ankhondo aja, adasangalala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Pamene anthu onse amene Ismaeli anawagwira anaona Yohanani mwana wa Kareya pamodzi ndi atsogoleri a ankhondo amene anali naye, anasangalala.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 41:13
2 Mawu Ofanana  

anatenga anthu onse, nanka kukamenyena ndi Ismaele mwana wa Netaniya, nampeza pamadzi ambiri a mu Gibiyoni.


Ndipo anthu onse amene Ismaele anatenga ndende kuwachotsa mu Mizipa anatembenuka nabwera, nanka kwa Yohanani mwana wake wa Kareya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa