Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 41:12 - Buku Lopatulika

12 anatenga anthu onse, nanka kukamenyena ndi Ismaele mwana wa Netaniya, nampeza pamadzi ambiri a mu Gibiyoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 anatenga anthu onse, nanka kukamenyena ndi Ismaele mwana wa Netaniya, nampeza pa madzi ambiri a m'Gibiyoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 adasonkhanitsa anthu onse amene anali nawo, napita kukamenyana naye nkhondo. Adakampeza ku chidziŵe cha ku Gibiyoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 anatenga ankhondo awo onse kupita kukamenyana ndi Ismaeli mwana wa Netaniya. Anakamupeza kufupi ndi chidziwe chachikulu cha ku Gibiyoni.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 41:12
5 Mawu Ofanana  

Ndi Yowabu mwana wa Zeruya, ndi anyamata a Davide anatuluka nakomana nao pa thamanda la Gibiyoni; nakhala pansi, ena tsidya lino, ndi ena tsidya lija la thamandalo.


Ndipo panali pamene anthu onse amene anali ndi Ismaele anaona Yohanani mwana wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala naye, anasekera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa